Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb17 January tsamba 4
  • “Inu Yehova, . . . Chikhulupiriro Changa Chili mwa Inu”

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • “Inu Yehova, . . . Chikhulupiriro Changa Chili mwa Inu”
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
  • Nkhani Yofanana
  • Pangani Yehova Kukhala Chikhulupiriro Chanu
    Nsanja ya Olonda—1988
  • Anatipatsa Ufulu Wosankha
    Nsanja ya Olonda—2010
  • Mulungu Athandiza Mfumu Hezekiya
    Bukhu Langa la Nkhani za Baibulo
  • “Anapitiriza Kumamatira Yehova”
    Nsanja ya Olonda—2012
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
mwb17 January tsamba 4

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

“Inu Yehova, . . . Chikhulupiriro Changa Chili mwa Inu”

Hezekiya akupemphera

Tiyenera kukhulupirira Yehova tikakhala pa mtendere ngakhalenso pa mavuto. (Sal. 25:1, 2) M’zaka za m’ma 700 B.C.E., Ayuda amene anali ku Yuda anakumana ndi mavuto omwe anayesa chikhulupiriro chawo. Tingaphunzire zambiri pa zomwe zinawachitikirazi. (Aroma 15:4) Kambiranani mafunso otsatirawa okhudza vidiyo yakuti “Inu Yehova, . . . Chikhulupiriro Changa Chili mwa Inu.”

  1. Kodi Hezekiya anakumana ndi mavuto otani?

  2. Kodi Hezekiya anagwiritsa ntchito bwanji mfundo ya pa Miyambo 22:3 pokonzekera kubwera kwa Asuri?

  3. N’chifukwa chiyani Hezekiya sanadzipereke kwa Asuri kapena kupanga mgwirizano ndi Aiguputo?

  4. N’chifukwa chiyani Hezekiya ndi chitsanzo chabwino kwa Akhristu?

  5. Kodi ndi zinthu ziti masiku ano zimene zingayese chikhulupiriro chathu?

Lembani mbali zimene mukuona kuti mukuyenera kumadalira kwambiri Yehova . . .

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena