Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb17 May tsamba 4
  • Yehova Sangaiwale Chikondi Chanu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Yehova Sangaiwale Chikondi Chanu
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
  • Nkhani Yofanana
  • Muziona Kuti Achikulire Okhulupirika Ndi Amtengo Wapatali
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2021
  • Yehova Amasamalira Mwachikondi Atumiki Ake Okalamba
    Nsanja ya Olonda—2008
  • Akristu Owona Amalemekeza Anthu Okalamba!
    Nsanja ya Olonda—1987
  • Muziona Kuti Achinyamata Ndi Amtengo Wapatali
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2021
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
mwb17 May tsamba 4

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

Yehova Sangaiwale Chikondi Chanu

ONERANI VIDIYO YAKUTI YEHOVA SANGAIWALE CHIKONDI CHANU, KENAKO YANKHANI MAFUNSO OTSATIRAWA:

  • Kodi munthu akamakalamba amakumana ndi mavuto otani?

  • Kodi ndi makhalidwe abwino ati amene okalamba ambiri amakhala nawo?

  • Ngati ndinu wokalamba, kodi malemba a Levitiko 19:32 ndi Miyambo 16:31 angakulimbikitseni bwanji?

  • Kodi Yehova amawaona bwanji atumiki ake okalamba omwe sangathe kuchita zambiri pomutumikira?

  • Kodi Yehova amafuna kuti tizichita chiyani ngakhale titakalamba?

  • Kodi okalamba angalimbikitse bwanji achinyamata?

  • Kodi posachedwapa m’bale kapena mlongo wokalamba wakulimbikitsani bwanji?

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena