Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb17 June tsamba 4
  • Mtima Wodikira Umatithandiza Kuti Tipirire

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Mtima Wodikira Umatithandiza Kuti Tipirire
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
  • Nkhani Yofanana
  • Sonyezani Mtima Wodikira!
    Nsanja ya Olonda—2000
  • Osangalala Kudikira Yehova
    Nsanja ya Olonda—2007
  • Mfundo Zazikulu za M’buku la Maliro
    Nsanja ya Olonda—2007
  • ‘Mudzandiweramira Kuti Mundithandize’
    Nsanja ya Olonda—2012
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
mwb17 June tsamba 4

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | MALIRO 1-5

Mtima Wodikira Umatithandiza Kuti Tipirire

Kodi n’chiyani chinathandiza kuti Yeremiya apirire ngakhale kuti anakumana ndi mavuto aakulu?

3:20, 21, 24, 26, 27

  • Iye ankakhulupirira ndi mtima wonse kuti Yehova ‘adzaweramira’ anthu ake omwe analapa n’kuwapulumutsa m’mavuto awo

  • Iye anaphunzira ‘kunyamula goli lake ali mnyamata.’ Munthu akamapirira mayesero ali wamng’ono zimamuthandiza kuti adzathe kupirira mavuto omwe angadzakumane nawo m’tsogolo

Yeremiya akupemphera ataona kuti anthu a ku Yerusalemu atengedwa kupita kuukapolo

Kodi ndingakonzekere bwanji mavuto amene ndingakumane nawo m’tsogolo?

Kodi ndingasonyeze bwanji kuti ndili ndi mtima wodikira?

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena