Akulalikira ku Tonga
Zimene Tinganene
●○○ ULENDO WOYAMBA
Funso: Kodi tingadziwe bwanji zinthu zomwe zidzachitike m’tsogolo?
Lemba: Yes. 46:10
Funso la Ulendo Wotsatira: Kodi Mulungu amatilonjeza zotani zokhudza m’tsogolo komanso dziko lapansili?
○●○ ULENDO WOBWEREZA WOYAMBA
Funso: Kodi Mulungu amatilonjeza zotani zokhudza m’tsogolo komanso dziko lapansili?
Lemba: Sal. 37:29
Funso la Ulendo Wotsatira: Kodi tingatani kuti tidzaone nawo kukwaniritsidwa kwa malonjezo a m’Baibulo?
○○● ULENDO WOBWEREZA WACHIWIRI
Funso: Kodi tingatani kuti tidzaone nawo kukwaniritsidwa kwa malonjezo a m’Baibulo?
Lemba: Sal. 37:34
Funso la Ulendo Wotsatira: Kodi Mulungu amafuna kuti tizichita chiyani pa moyo wathu?