Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb18 October tsamba 2
  • Yesu Amasamalira Nkhosa Zake

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Yesu Amasamalira Nkhosa Zake
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2018
  • Nkhani Yofanana
  • Amene Angatitonthoze
    Phunzirani kwa Mphunzitsi Waluso
  • Mbusa Wachikondi
    Kumamumvetsera Mphunzitsi Wamkuru’yo
  • Abusa Achikondi, Nkhosa Zokhulupirira
    Galamukani!—1988
  • “Nkhosa Zosochera Ndidzazifunafuna”
    Bwererani kwa Yehova
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2018
mwb18 October tsamba 2

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | YOHANE 9-10

Yesu Amasamalira Nkhosa Zake

10:1-5, 11, 14, 16

Yesu yemwe ndi m’busa wabwino, amadziwa bwino nkhosa zake. Amadziwa zomwe timafuna, zimene timachita bwino komanso zimene timalephera. Nazonso nkhosa zimadziwa bwino m’busa wawo komanso zimamudalira akamazitsogolera.

Kodi Yesu amakhala bwanji m’busa wabwino pankhani . . .

  • yosonkhanitsa nkhosa zake?

  • yotsogolera nkhosa zake?

  • yoteteza nkhosa zake?

  • yodyetsa nkhosa zake?

M’busa akulondera khola la nkhosa

FUNSO LOFUNIKA KULIGANIZIRA: Kodi ndingasonyeze bwanji kuti ndimayamikira zimene Yesu amachita pondisamalira?

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena