Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb18 December tsamba 3
  • Baranaba ndi Paulo Ankathandiza Anthu Kukhala Ophunzira M’madera Akutali Kwambiri

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Baranaba ndi Paulo Ankathandiza Anthu Kukhala Ophunzira M’madera Akutali Kwambiri
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2018
  • Nkhani Yofanana
  • Barnaba—“Mwana wa Chitonthozo”
    Nsanja ya Olonda—1998
  • “Anapitiriza Kukhala Osangalala Komanso Mzimu Woyera Unkawathandiza Kwambiri”
    ‘Kuchitira Umboni Mokwanira za Ufumu wa Mulungu’
  • Anthu a Yehova Alimbitsidwa m’Chikhulupiriro
    Nsanja ya Olonda​—1990
  • Chitsanzo Chouziridwa cha Ntchito Yaumishonale Wachikristu
    Nsanja ya Olonda—1992
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2018
mwb18 December tsamba 3
Paulo ndi Baranaba ali kwa Serigio Paulo

Paulo ndi Baranaba ali kwa Serigio Paulo

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | MACHITIDWE 12-14

Baranaba ndi Paulo Ankathandiza Anthu Kukhala Ophunzira M’madera Akutali Kwambiri

13:12, 48; 14:1, 21, 22

Baranaba ndi Paulo anagwira ntchito mwakhama pothandiza anthu kuti akhale Akhristu ngakhale kuti ankatsutsidwa kwambiri

  • Ankalalikira anthu a mitundu yosiyanasiyana

  • Ankalimbikitsa ophunzira atsopano kuti “akhalebe m’chikhulupiriro”

Sitingathe kudziwa anthu omwe ali ndi ‘maganizo abwino amene angawathandize kudzapeza moyo wosatha’ pokhapokha titawalalikira, mwinanso maulendo ambirimbiri. Choncho timalalikira anthu onse mopanda tsankho.

Kodi ndi ndani amene ndingamupemphe kuti ndiziphunzira naye Baibulo mlungu uno?

Kodi ndi njira zina ziti zimene ndingalimbikitsire Akhristu anzanga kuti “akhalebe m’chikhulupiriro”?

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena