Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb20 February tsamba 8
  • Yehova Amakwaniritsa Zomwe Walonjeza

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Yehova Amakwaniritsa Zomwe Walonjeza
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
  • Nkhani Yofanana
  • Abrahamu ndi Sara Mungatsanzire Chikhulupiriro Chawo!
    Nsanja ya Olonda—2004
  • Kodi N’kusungiranji Malonjezo Anu?
    Nsanja ya Olonda—1999
  • Kodi Tingatani Kuti Tizikhulupirira Kwambiri Lonjezo la Yehova la Dziko Latsopano?
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2023
  • Mtambo Waukulu Wotere wa Mboni!
    Nsanja ya Olonda—1987
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
mwb20 February tsamba 8
Sara ali woyembekezera; Sara wagwira Isaki ndipo akuyang’ana Hagara ndi Isimaeli pamene akuyenda kulowera m’chipululu.

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | GENESIS 20-21

Yehova Amakwaniritsa Zomwe Walonjeza

21:1-3, 5-7, 10-12, 14

Yehova anadalitsa Abulahamu ndi Sara chifukwa cha chikhulupiriro chawo powapatsa mwana wamwamuna. Patapita nthawi, kumvera kwawo pamene ankakumana ndi mayesero kunasonyeza kuti ankakhulupirira malonjezo a Yehova a m’tsogolo.

Kodi zomwe ndimachita ndikakumana ndi mayesero zimasonyeza bwanji kuti ndimakhulupirira malonjezo a Yehova? Nanga ndingalimbitse bwanji chikhulupiriro changa?

Mlongo wagonekedwa m’chipatala ndipo akukambirana ndi dokotala zokhudza magazi ndipo mwamuna komanso mwana wake wamkazi ali pambali.
    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena