Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb20 November tsamba 3
  • Chifukwa Chake Nsembe Zinkaperekedwa

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Chifukwa Chake Nsembe Zinkaperekedwa
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
  • Nkhani Yofanana
  • Nsembe Zotamanda Zimene Zimakondweretsa Yehova
    Nsanja ya Olonda—2000
  • Nsembe Zimene Zinakondweretsa Mulungu
    Nsanja ya Olonda—2000
  • Kupereka Nsembe Zokondweretsa Mulungu
    Nsanja ya Olonda—2007
  • Phunzirani Kuchokera ku Choonadi cha M’chilamulo
    Nsanja ya Olonda—2012
Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
mwb20 November tsamba 3
1. Ng’ombe, nkhosa ndi mbuzi zoti ziperekedwe nsembe. 2. Yesu wapachikidwa pamtengo wozunzikirapo

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | LEVITIKO 1-3

Chifukwa Chake Nsembe Zinkaperekedwa

1:3; 2:1, 12; 3:1

Nsembe zimene zinkaperekedwa mogwirizana ndi Chilamulo zinkasangalatsa Yehova komanso zinkaimira nsembe ya dipo ya Yesu kapena madalitso amene nsembeyo idzabweretse.​—Ahe 8:3-5; 9:9; 10:5-10.

  • Mofanana ndi mmene nyama zimene zinkaperekedwa nsembe zinkayenera kukhala zopanda chilema, Yesu anapereka nsembe thupi lake langwiro, lopanda vuto lililonse​—1Pe 1:18, 19; onani chithunzi chapachikuto

  • Mofanana ndi nsembe zopsereza zomwe zinkaperekedwa zathunthu kwa Mulungu, Yesu anapereka moyo wake wonse kwa Yehova

  • Mofanana ndi mmene anthu omwe ankapereka nsembe zachiyanjano zovomerezeka analili pa mtendere ndi Mulungu, odzozedwa amene amadya zizindikiro pa Chakudya Chamadzulo cha Ambuye amakhala pa mtendere ndi Mulungu

M’bale wodzozedwa akudya mkate pa nthawi ya Chakudya Chamadzulo cha Ambuye.
    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena