Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb21 May tsamba 6
  • Thawirani kwa Yehova

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Thawirani kwa Yehova
  • Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2021
  • Nkhani Yofanana
  • Yehova Amaona Kuti Moyo wa Munthu Ndi Wamtengo Wapatali
    Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2021
  • Midzi Yopulumukirako—Makonzedwe Achifundo A Mulungu
    Nsanja ya Olonda—1995
  • Kodi Mumathawira kwa Yehova?
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2017
  • “Nyamulani Mwana Wanu”
    Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2022
Onani Zambiri
Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2021
mwb21 May tsamba 6

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

Thawirani kwa Yehova

Mu Isiraeli munali mizinda 6 yoti amene wapha munthu mwangozi azithawirako (Nu 35:15; w17.11 9 ¶4)

Akulu a mu Isiraeli ankaweruza mlandu uliwonse (Nu 35:24; w17.11 9 ¶6)

Mizinda yothawirako inali malo achitetezo (Nu 35:25; w17.11 11 ¶13)

Mofanana ndi munthu yemwe wapha mnzake mwangozi amene ankafunika kusiya moyo umene anazolowera kuti akhale ndi mwayi wotetezedwa ndi mizinda yothawirako, ifenso timafunika kusiya zinthu zina kuti Yehova atichitire chifundo n’kutikhululukira.

Wachinyamata wawerama ndipo akudzimvera chisoni. Zithunzi zosonyeza anthu omwe akufuna kuti Yehova awakhululukire: 1. Wochimwa yemwe walapa akufotokoza mlandu wake kwa akulu a mzinda wothawirako. 2.Wachinyamata wolapa yemwe amadzimvera chisoni uja akukumana ndi akulu awiri.
    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena