Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb21 July tsamba 16
  • Kukhala Olimba Mtima Sikovuta Kwambiri

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kukhala Olimba Mtima Sikovuta Kwambiri
  • Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2021
  • Nkhani Yofanana
  • ‘Limba Mtima Ndipo Ugwire Ntchitoyi’
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2017
  • Khalani Olimba Mtima!
    Nsanja ya Olonda—1993
  • ‘Khalani Olimba Mtima Kwambiri Ndipo Muchite Zinthu Mwamphamvu’
    Nsanja ya Olonda—2012
  • Ndithandizeni Ndikhale Wolimba Mtima
    Imbirani Yehova Mosangalala
Onani Zambiri
Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2021
mwb21 July tsamba 16
Mlongo akulalikira mnzake wa kusukulu molimba mtima pogwiritsa ntchito foni.

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

Kukhala Olimba Mtima Sikovuta Kwambiri

Munthu wolimba mtima amakhala wamphamvu komanso saopa. Koma izi sizikutanthauza kuti iye sakhaliratu wopanda mantha. M’malomwake, zikutanthauza kuti iye amachitabe zimene akufunika kuchitazo ngakhale kuti akuchita mantha. Yehova ndi amene amatithandiza kukhala olimba mtima. (Sl 28:7) Kodi achinyamata angasonyeze bwanji kulimba mtima?

ONERANI VIDIYO YAKUTI MUSAMATSANZIRE ANTHU AMANTHA, KOMA OLIMBA MTIMA, NDIPO KENAKO YANKHANI MAFUNSO OTSATIRAWA:

  • Kodi achinyamata amakumana ndi zinthu ziti zimene zimafunika kulimba mtima?

  • Kodi ndi nkhani za m’Baibulo ziti zimene zingatithandize kukhala olimba mtima?

  • Kodi kulimba mtima kumathandiza bwanji ifeyo komanso anthu ena omwe akutiona?

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena