Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb22 March tsamba 8
  • Kodi Mungatani Kuti Mukhale Bwenzi Labwino?

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kodi Mungatani Kuti Mukhale Bwenzi Labwino?
  • Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2022
  • Nkhani Yofanana
  • Mulungu Akukuitanani Kuti Mukhale Bwenzi Lake
    Mungathe Kukhala Bwenzi la Mulungu!
  • Kodi Ndikaulule Tchimo la Mnzanga?
    Galamukani!—2008
  • Kodi Mungatani Kuti Mukhale Bwenzi Labwino?
    Galamukani!—2014
  • Kodi Baibulo Limanena Zotani pa Nkhani Yokhala Ndi Anzathu?
    Kuyankha Mafunso a M’Baibulo
Onani Zambiri
Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2022
mwb22 March tsamba 8

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

Kodi Mungatani Kuti Mukhale Bwenzi Labwino?

Muzitonthoza komanso kulimbikitsa mnzanu amene akuda nkhawa (1Sa 20:1, 2; w19.11 7 ¶18)

Muzichenjeza mnzanu ku zinthu zoopsa (1Sa 20:12, 13; w08 2/15 8 ¶7)

Muzimuikira kumbuyo ena akamamunenera zoipa (1Sa 20:30-32; w09 10/15 19 ¶11)

Banja likumvetsera m’bale amene akufunikira thandizo.

Anthu a Yehova ali ndi mwayi waukulu wokhala ndi anzawo abwino. Kuti tikhale ndi mabwenzi, tiyenera kukhala aubwenzi. Kodi ndi ndani amene mungakonde kuti akhale mnzanu mumpingo?

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena