Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb22 May tsamba 5
  • “Chikondi . . . Sichikondwera ndi Zosalungama”

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • “Chikondi . . . Sichikondwera ndi Zosalungama”
  • Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2022
  • Nkhani Yofanana
  • Akhristu Oona Amadziwika Chifukwa cha Chikondi​—Muzisangalala ndi Choonadi
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2018
  • Ogwirizana Pansi pa Mbendera ya Chikondi
    Nsanja ya Olonda—1989
  • Jonatani Anachita Zinthu Mothandizidwa ndi Mulungu
    Nsanja ya Olonda—2007
  • Yonatani Anali Wolimba Mtima Komanso Wokhulupirika
    Zimene Tingaphunzire Munkhani za M’Baibulo
Onani Zambiri
Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2022
mwb22 May tsamba 5

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

“Chikondi . . . Sichikondwera ndi Zosalungama”

Zinthu zonse zimene Akhristu oona amachita, zimatsogoleredwa ndi chikondi. Chikondi “Sichikondwera ndi zosalungama.” (1Ak 13:4, 6) Choncho tiyenera kupeweratu zosangalatsa zimene zimalimbikitsa zachiwerewere komanso zachiwawa. Ndiponso sitimasangalala anthu ena akamakumana ndi zinthu zoipa, ngakhale amene anatilakwira.​—Miy 17:5.

ONERANI VIDIYO YAKUTI MUZIKUMBUKIRA ZIMENE CHIKONDI CHIMACHITA KOMANSO ZIMENE SICHICHITA​—SICHIKONDWERA NDI ZOSALUNGAMA, KENAKO YANKHANI MAFUNSO OTSATIRAWA:

  • Kodi Davide anatani atauzidwa kuti Yonatani ndi Sauli aphedwa?

  • Kodi ndi nyimbo yoimba polira iti imene Davide anapekera Sauli ndi Yonatani?

  • N’chifukwa chiyani Davide sanasangalale atamva kuti Sauli wamwalira?

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena