Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • wp23 No. 1 tsamba 16
  • Mulungu Akulonjeza Kuti Kuvutika Maganizo Kudzatheratu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Mulungu Akulonjeza Kuti Kuvutika Maganizo Kudzatheratu
  • sanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yogawira)—2023
  • Nkhani Yofanana
  • Matenda Ovutika Maganizo Ndi Vuto la Padziko Lonse
    sanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yogawira)—2023
  • Zimene Muyenera Kudziwa Zokhudza Matenda a Muubongo
    Galamukani!—2014
  • “Zinthu Zakale Sizidzakumbukiridwanso”
    Nsanja ya Olonda—2012
  • Nsautso ya Maganizo Pamene Yakantha Mkristu
    Nsanja ya Olonda—1988
Onani Zambiri
sanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yogawira)—2023
wp23 No. 1 tsamba 16
Wa Mboni za Yehova akuphunzira Baibulo ndi mzimayi yemwe akuonekanso patsamba loyamba.

Mulungu Akulonjeza Kuti Kuvutika Maganizo Kudzatheratu

Kudzera m’Baibulo, Mulungu amapereka malangizo komanso amatonthoza anthu amene akuvutika ndi matenda amaganizo.

Kuwonjezera pamenepo, iye akulonjeza kuti adzathetseratu zinthu zimene zimachititsa kuti anthu azivutika ndi matenda amaganizo.

Mulungu akadzakwaniritsa lonjezo limeneli, sitidzamvanso kuwawa kulikonse, kuvutika ndi nkhawa kapena maganizo oipa chifukwa “zinthu zakale sizidzakumbukiridwanso ndipo sizidzabweranso mumtima.”​—Yesaya 65:17.

A Mboni za Yehova adzasangalala kukuthandizani kudziwa nthawi imene Mulungu adzakwaniritse lonjezo lokhazika mtima pansi limeneli komanso mmene adzachitire zimenezi.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena