Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w24 December tsamba 32
  • Anthu Okhulupirika kwa Yehova Amakwaniritsa Zimene Alonjeza

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Anthu Okhulupirika kwa Yehova Amakwaniritsa Zimene Alonjeza
  • Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2024
  • Nkhani Yofanana
  • “Uzikwaniritsa Zinthu Zimene Walonjeza”
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2017
  • Yehova Amadalitsa Anthu Okhulupirika
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2016
  • Mafunso Ochokera kwa Oŵerenga
    Nsanja ya Olonda—2002
  • Ankakondedwa Ndi Mulungu Komanso Anzake
    Nsanja ya Olonda—2011
Onani Zambiri
Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2024
w24 December tsamba 32

ZOTI NDIPHUNZIRE

Anthu Okhulupirika kwa Yehova Amakwaniritsa Zimene Alonjeza

Werengani Oweruza 11:30-40 kuti muone zimene mukuphunzira kwa Yefita ndi mwana wake wamkazi pa nkhani yokwaniritsa malonjezo.

Ganizirani nkhani yonse. Kodi Aisiraeli okhulupirika ankaona bwanji zimene amulonjeza Yehova? (Num. 30:2) Kodi Yefita ndi mwana wake wamkazi anasonyeza bwanji kuti ankakhulupirira Yehova?​—Ower. 11:9-11, 19-24, 36.

Fufuzani mozama. Kodi Yefita analonjeza chiyani nanga ankatanthauza chiyani? (w16.04 7 ¶12) Kodi Yefita ndi mwana wake anadzimana zinthu ziti kuti akwaniritse zimene analonjeza? (w16.04 7-8 ¶14-16) Kodi ndi zinthu ziti zimene Akhristu angalonjeze masiku ano?​—w17.04 5-8 ¶10-19.

Onani zimene mukuphunzirapo. Dzifunseni kuti:

  • ‘N’chiyani chingandithandize kukwaniritsa lonjezo lomwe ndinachita podzipereka kwa Yehova?’ (w20.03 13 ¶20)

  • ‘Kodi ndingadzimane zinthu ziti kuti ndizichita zambiri potumikira Yehova?’

  • ‘Kodi ndingatani kuti ndizikwaniritsa zimene ndinalonjeza mwamuna kapena mkazi wanga pamene tinkakwatirana?’ (Mat. 19:5, 6; Aef. 5:28-33)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena