Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • wp25 No. 1 tsamba 16
  • Kodi Munayamba Mwadzifunsapo Mafunso Otsatirawa?

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kodi Munayamba Mwadzifunsapo Mafunso Otsatirawa?
  • Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yogawira)—2025
  • Nkhani Yofanana
  • Mtendere Weniweni—Kodi Udzachokera Kuti?
    Nsanja ya Olonda—1997
  • Mtendere wa Umulungu Kaamba ka Awo Ophunzitsidwa ndi Yehova
    Nsanja ya Olonda—1987
  • Lolani “Mtendere wa Mulungu” Uchinjirize Mtima Wanu
    Nsanja ya Olonda—1991
Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yogawira)—2025
wp25 No. 1 tsamba 16
Msilikali wanyamula mfuti ndipo akuganizira akuyenda m’munda m’dziko lamtendere komanso lokongola limodzi ndi mkazi komanso mwana wake.

Kodi Munayamba Mwadzifunsapo Mafunso Otsatirawa?

  • Popeza kuti aliyense amafuna mtendere, n’chifukwa chiyani padzikoli pakuchitika nkhondo?

  • Kodi n’zotheka kukhala mwamtendere m’dziko limene mukuchitika zachiwawa?

  • Kodi padzakhala nthawi imene sikudzakhalanso nkhondo?

Mukhoza kudabwa ndi mayankho a m’Baibulo a mafunso amenewa ndipo mosakayikira mayankhowo angakulimbikitseni kwambiri.

Mungachitenso bwino kufufuza nokha zimene Baibulo limanena pa nkhani yofunika kwambiriyi. Kuti mudziwe zambiri, werengani magazini ya Nsanja ya Olonda ino.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena