Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • yb14 tsamba 8-9
  • Zimene Zachitika M’chaka Chapitachi

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zimene Zachitika M’chaka Chapitachi
  • Buku Lapachaka la Mboni za Yehova 2014
  • Nkhani Yofanana
  • Gareta Lakumwamba la Yehova Likuyenda
    Nsanja ya Olonda—1991
  • Kodi Ntchito Yomanga Ikuyenda Bwanji ku Warwick?
    Buku Lapachaka la Mboni za Yehova la 2016
  • Yenderani Limodzi ndi Gareta Lakumwamba la Yehova
    Nsanja ya Olonda—1991
  • “Ndinayamba Kuona Masomphenya a Mulungu”
    Yehova Wabwezeretsa Kulambira Koyera
Onani Zambiri
Buku Lapachaka la Mboni za Yehova 2014
yb14 tsamba 8-9

Zimene Zachitika M’chaka Chapitachi

Yehova anaonetsa Ezekieli masomphenya a galeta lalikulu lakumwamba. Galeta limeneli likuimira mbali yosaoneka ya gulu la Yehova. Ngakhale kuti galetali ndi lalikulu kwambiri, likuthamanga pa liwiro lalikulu ndipo likutha kukhotera kwina kulikonse mofulumira kwambiri. (Ezek. 1:15-28) Zinthu zosangalatsa zimene zachitika m’chaka chapitachi zikusonyeza kuti mbali yapadziko lapansi ya gulu la Yehova Mulungu ilinso pa liwiro lalikulu.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena