Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • ijwfq nkhani 14
  • Kodi mipingo ya Mboni za Yehova imayendetsedwa bwanji?

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kodi mipingo ya Mboni za Yehova imayendetsedwa bwanji?
  • Mafunso Ofunsidwa Kawirikawiri
  • Nkhani Yofanana
  • Oyang’anira Oyendayenda—Mphatso mwa Amuna
    Nsanja ya Olonda—1996
  • Kodi Ntchito Yomanga Ikuyenda Bwanji ku Warwick?
    Buku Lapachaka la Mboni za Yehova la 2016
  • Kodi Oyang’anira Dera Amatithandiza Bwanji?
    Kodi Ndani Akuchita Chifuniro cha Yehova Masiku Ano?
  • “Pitirizani Kusunga Amuna Oterowo Okondedwa”
    Nsanja ya Olonda—1988
Onani Zambiri
Mafunso Ofunsidwa Kawirikawiri
ijwfq nkhani 14
Msonkhano wa mpingo

Kodi mipingo ya Mboni za Yehova imayendetsedwa bwanji?

Mpingo uliwonse umayendetsedwa ndi bungwe la akulu. Mipingo pafupifupi 20 imapanga dera ndipo madera pafupifupi 10 amapanga chigawo. Nthawi ndi nthawi, mpingo uliwonse umachezeredwa ndi akulu ena amene amayendera mipingo, omwe timawatchula kuti oyang’anira madera ndiponso oyang’anira zigawo.

Mipingo imalandira malangizo a m’Baibulo ochokera ku Bungwe Lolamulira. Bungweli lapangidwa ndi a Mboni amene atumikira Mulungu kwa nthawi yaitali, omwe panopa ali kumaofesi a Mboni za Yehova a ku Brooklyn, mumzinda wa New York ku America. Maofesi amenewa ndi likulu la Mboni za Yehova padziko lonse.—Machitidwe 15:23-29; 1 Timoteyo 3:1-7.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena