-
Genesis 46:2Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
2 Ndiyeno Mulungu analankhula ndi Isiraeli mʼmasomphenya usiku kuti: “Yakobo, Yakobo!” Ndipo Yakobo anayankha kuti: “Ine mbuyanga!”
-