-
Genesis 19:35Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
35 Choncho usiku umenewonso anakhala akuwapatsa vinyo bambo awo kuti azimwa. Kenako, mwana wamngʼono uja anapita nʼkukagona nawo. Koma kuyambira pamene mwanayo anapita kukagona nawo mpaka pamene anachoka, bambowo sanadziwe chilichonse.
-