-
Genesis 24:14Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
14 Zichitike kuti, mtsikana amene ndimuuze kuti, ‘Chonde tula pansi mtsuko wako wa madzi kuti ndimweko,’ ndipo iye nʼkundiyankha kuti, ‘Imwani, ndiponso nditungira madzi ngamila zanu kuti zimwe,’ ameneyo akhale amene mwasankhira mtumiki wanu Isaki. Mukachita zimenezo, ndidziwa kuti mwasonyeza chikondi chokhulupirika kwa mbuye wanga.”
-