Ekisodo 6:20 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 20 Tsopano Amuramu anatenga Yokebedi, mchemwali wa bambo ake, kukhala mkazi wake.+ Ndipo Yokebedi anamʼberekera Amuramu, Aroni ndi Mose.+ Amuramu anakhala ndi moyo zaka 137.
20 Tsopano Amuramu anatenga Yokebedi, mchemwali wa bambo ake, kukhala mkazi wake.+ Ndipo Yokebedi anamʼberekera Amuramu, Aroni ndi Mose.+ Amuramu anakhala ndi moyo zaka 137.