-
Ekisodo 15:22Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
22 Kenako Mose anatsogolera Isiraeli kuchoka ku Nyanja Yofiira ndipo analowa mʼchipululu cha Shura. Iwo anayenda mʼchipululumo kwa masiku atatu, koma sanapeze madzi.
-