Ekisodo 18:5 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 5 Choncho Yetero, apongozi ake a Mose, limodzi ndi ana aamuna a Mose ndi mkazi wake, anapita kwa Mose mʼchipululu, kuphiri la Mulungu woona, kumene anamanga msasa.+
5 Choncho Yetero, apongozi ake a Mose, limodzi ndi ana aamuna a Mose ndi mkazi wake, anapita kwa Mose mʼchipululu, kuphiri la Mulungu woona, kumene anamanga msasa.+