Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 35:35
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 35 Iye wawapatsa luso*+ kuti agwire ntchito zonse. Wawapatsa luso lopeta nsalu komanso luso loluka nsalu ndi ulusi wabuluu, ubweya wa nkhosa wapepo, ulusi wofiira kwambiri, nsalu zabwino kwambiri ndi luso lowomba nsalu. Amuna amenewa adzagwira ntchito iliyonse komanso kukonza kapangidwe ka zinthu zosiyanasiyana.”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena