-
Levitiko 15:3Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
3 Iye ndi wodetsedwa chifukwa cha zimene zikukhazo, kaya zinthuzo zikupitirizabe kutuluka kapena maliseche ake atsekeka ndi zimene zikukhazo, azikhalabe wodetsedwa.
-