-
Levitiko 25:4Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
4 Koma mʼchaka cha 7 dzikolo lizidzasunga sabata lopuma pa zonse, sabata la Yehova. Musamadzadzale mbewu mʼminda yanu kapena kudulira mitengo yanu ya mpesa.
-