21 Lamulo lokhudza Mnaziri+ amene wachita lonjezo ndi ili: Ngati analonjeza ndipo angakwanitse kupereka nsembe kwa Yehova, kuwonjezera pa zimene amayenera kupereka monga Mnaziri, azikwaniritsa lonjezo lake, posonyeza kuti akulemekeza lamulo la unaziri wake.’”