38 Zofukizira za amuna amene anafa chifukwa cha kuchimwa kwawo azisule kuti zikhale timalata topyapyala ndipo mukutire guwa lansembe.+ Zofukizirazo zinakhala zopatulika chifukwa anafika nazo pamaso pa Yehova. Ndiye timalatato tikhale chikumbutso kwa Aisiraeli.”+