-
Numeri 21:28Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
28 Chifukwa moto unatuluka ku Hesiboni, lawi lamoto linatuluka mʼtauni ya Sihoni.
Wawotcha Ari mzinda wa ku Mowabu, wawotcha olamulira amʼmalo okwezeka a ku Arinoni.
-