-
Numeri 31:50Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
50 Choncho tiloleni kuti aliyense wa ife apereke zinthu zimene wabwera nazo monga chopereka kwa Yehova. Tabwera ndi zinthu zagolide, matcheni ovala mʼmiyendo, zibangili, mphete zachifumu, ndolo ndi zodzikongoletsera zina. Tipereka zimenezi kwa Yehova kuti ziphimbe machimo athu.”
-