-
Deuteronomo 3:3Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
3 Choncho Yehova Mulungu wathu anaperekanso Ogi mfumu ya Basana ndi anthu ake onse mʼmanja mwathu, ndipo tinawapha moti panalibe munthu ngakhale mmodzi mwa anthu ake, yemwe anapulumuka.
-