-
Deuteronomo 6:21Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
21 mwana wanuyo mudzamuyankhe kuti, ‘Tinali akapolo a Farao ku Iguputo, koma Yehova anatitulutsa ku Iguputoko ndi dzanja lamphamvu.
-