-
Deuteronomo 13:5Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
5 Koma mneneri kapena woloserayo muzimupha,+ chifukwa akulimbikitsa anthu kuti azipandukira Yehova Mulungu wanu amene anakutulutsani mʼdziko la Iguputo komanso kukuwombolani mʼnyumba yaukapolo. Munthu ameneyo akufuna akupatutseni panjira imene Yehova Mulungu wanu anakulamulani kuti muziyendamo. Choncho muzichotsa woipayo pakati panu.+
-