-
Deuteronomo 30:13Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
13 Ndiponso silili tsidya lina la nyanja kuti munene kuti, ‘Ndani adzawoloke kupita tsidya lina la nyanja kuti akatitengere lamulolo kuti ife tidzalimve nʼkulitsatira?’
-