21 Ndiyeno akadzakumana ndi masoka komanso mavuto ambiri,+ nyimboyi idzawakumbutsa zimene ndinawachenjeza, (chifukwa mbadwa zawo sizikuyenera kuiwala nyimboyi), chifukwa ndikudziwa kale mtima umene ayamba kukhala nawo+ ndisanawalowetse nʼkomwe mʼdziko limene ndinawalumbirira.”