Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yoswa 8:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Tsopano mfumu ya Ai itaona zimenezo, nthawi yomweyo mfumuyo ndi amuna amumzindawo anakonzeka kuti akamenyane ndi Aisiraeli. Anadzuka mʼmamawa kukakumana nawo pamalo ena pomwe ankatha kuona bwino chigwa cha mʼchipululu. Koma mfumuyo sinadziwe kuti asilikali ena anali atabisala kumbuyo kwa mzindawo.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena