Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Oweruza 5:30
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 30 ‘Ayenera kuti akugawa zinthu zimene apeza,

      Akugawa mtsikana mmodzi, kapena atsikana awiri kwa msilikali aliyense,

      Nsalu zokongola za Sisera, ndithu nsalu zokongola,

      Chovala chopeta chokongola, inde, zovala ziwiri zopeta,

      Zoti amuna omwe alanda zinthu avale mʼmakosi awo.’

  • Oweruza
    Buku Lofufuzira Nkhani la Mboni za Yehova la 2019
    • 5:30

      Nsanja ya Olonda,

      8/1/2015, tsa. 13

      11/15/2003, tsa. 31

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena