-
Oweruza 11:33Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
33 Iye anapha Aamoni ambirimbiri mʼmizinda 20, kuyambira ku Aroweli mpaka ku Miniti ndipo anakafikanso ku Abele-kerami. Choncho Aisiraeli anagonjetsa Aamoni.
-