-
Oweruza 16:14Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
14 Iye anamangadi zingongozo nʼkuzipina. Kenako anamuuza kuti: “Afilisiti aja abwera Samisoni!” Samisoni atamva zimenezi anadzuka ndipo anachotsa chopinira chija komanso ulusi uja.
-