Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Oweruza 18:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Choncho amuna 5 aja anapitiriza ulendo wawo ndipo anafika mumzinda wa Laisi.+ Anaona kuti anthu amumzindawo ankakhala mosadalira aliyense, ngati mmene ankakhalira Asidoni. Iwo ankakhala mosatekeseka+ ndipo panalibe amene anawagonjetsa nʼkumawalamulira mwankhanza kapena kuwasokoneza. Ankakhala kutali kwambiri ndi Asidoni ndipo sankayenderana ndi anthu ena.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena