Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Oweruza 20:28
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 28 Masiku amenewo Pinihasi,+ mwana wa Eliezara, mwana wa Aroni, ndi amene ankatumikira* pafupi ndi likasalo. Choncho amuna a Isiraeli anafunsa kuti: “Kodi tipitenso kukamenyana ndi abale athu a fuko la Benjamini kapena basi tisapitenso?”+ Yehova anayankha kuti: “Pitani, chifukwa mawa ndiwapereka mʼmanja mwanu.”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena