4 Ndiye ine ndaganiza zoti ndikuuze kuti, ‘Ugule malowo pamaso pa anthu ndiponso pamaso pa akulu a mzindawu.+ Ngati ukufuna kuwawombola, awombole. Koma ngati sukufuna undiuze, chifukwa iweyo ndiye woyenera kuwombola malowo ndipo pambuyo pako pali ineyo.’” Iye anayankha kuti: “Ndiwombola ineyo.”+