-
1 Samueli 19:10Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
10 Sauli anafuna kubaya Davide ndi mkondo kuti amukhomerere kukhoma. Koma Davide anauzinda moti mkondowo unalasa khoma. Usiku umenewo Davide anathawa.
-