Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Samueli 3:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Abineri atamva mawu a Isi-bosetiwa anakwiya kwambiri ndipo anati: “Kodi ndine galu wopanda pake wa Yuda? Ineyo ndakhala ndikusonyeza chikondi chokhulupirika kwa anthu a nyumba ya Sauli bambo ako, azichimwene ake komanso anzake ndipo sindinakupereke mʼmanja mwa Davide. Koma lero ukundiimba mlandu pa zimene ndinalakwitsa zokhudza mkazi.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena