-
2 Samueli 10:8Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
8 Ndiyeno Aamoni anapita kukaima pageti la mzinda atakonzekera kumenya nkhondo. Pomwe Asiriya a ku Zoba, a ku Rehobu, a ku Isitobu ndi a ku Maaka anakayalana kwaokha kutchire.
-