Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Samueli 19:43
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 43 Koma anthu a ku Isiraeli anayankha anthu a ku Yuda kuti: “Ifetu tili ndi mafuko 10 mu ufumu wa Davide, choncho tili ndi mphamvu zambiri kuposa inuyo. Ndiye nʼchifukwa chiyani mwatinyoza chonchi? Kodi ife sitinayenera kukhala patsogolo pobweretsa mfumu yathu?” Koma anthu a ku Isiraeliwo anagonja chifukwa cha zimene anthu a ku Yuda ananena.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena