Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Samueli 20:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Koma Amasa sanali tcheru ndi lupanga limene linali mʼmanja mwa Yowabu. Choncho Yowabuyo anamubaya nalo mʼmimba+ ndipo matumbo ake anakhuthukira pansi. Anangomubaya kamodzi nʼkuferatu, sanachite kumubaya kawiri. Kenako Yowabu ndi mchimwene wake Abisai anapitiriza kusaka Sheba mwana wa Bikiri.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena