Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Samueli 20:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Yowabu ndi asilikali ake* anafika nʼkuzungulira mzinda wa Abele wa ku Beti-maaka womwe unazunguliridwa ndi malo okwera amene anthu amumzindawo anamanga. Yowabu ndi asilikali ake anamanganso malo okwera omenyerapo nkhondo. Anthu onse amene anali ndi Yowabu ankakumba pansi pa mpandawo kuti augwetse.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena