-
2 Samueli 20:22Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
22 Nthawi yomweyo, mayi wanzeruyo anapita nʼkukalankhula ndi anthu onse, ndipo anthuwo anadula mutu wa Sheba mwana wa Bikiri nʼkuuponya kwa Yowabu. Zitatero, Yowabu analiza lipenga la nyanga ya nkhosa ndipo anthu onse anachoka kumzindawo nʼkupita kwawo.+ Yowabu nayenso anabwerera ku Yerusalemu kwa mfumu.
-