Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Samueli 20:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Nthawi yomweyo, mayi wanzeruyo anapita nʼkukalankhula ndi anthu onse, ndipo anthuwo anadula mutu wa Sheba mwana wa Bikiri nʼkuuponya kwa Yowabu. Zitatero, Yowabu analiza lipenga la nyanga ya nkhosa ndipo anthu onse anachoka kumzindawo nʼkupita kwawo.+ Yowabu nayenso anabwerera ku Yerusalemu kwa mfumu.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena