5 Kodi nyumba yanga siili choncho kwa Mulungu?
Chifukwa wachita nane pangano lomwe lidzakhalapo mpaka kalekale,+
Analikonza bwino ndipo ndi lotetezeka.
Chifukwa ndi chipulumutso changa ndipo limandisangalatsa,
Chimenechi ndiye chifukwa chake amakulitsa panganoli.+